-
Ezekieli 26:20Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
-
-
20 ndidzakutsitsira m’dzenje, ngati mmene ndinatsitsira ena onse m’manda momwe muli anthu amene anafa kalekale.+ Ine ndidzakuchititsa kukhala pansi, panthaka.+ Udzakhala kumeneko pamodzi ndi malo ena amene anawonongedwa kalekale ndiponso pamodzi ndi ena onse amene akutsikira kumanda.+ Ndidzachita zimenezi kuti anthu asadzakhalenso mwa iwe, koma m’dziko la anthu amoyo ndidzaikamo zokongoletsera.+
-