Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Genesis 50:26
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 26 Patapita nthawi, Yosefe anamwalira ali ndi zaka 110. Thupi lake analikonza ndi mankhwala kuti lisawonongeke,+ ndipo analiika m’bokosi ku Iguputoko.

  • Yesaya 22:16
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 16 ‘Kodi kuno kuli wachibale wako aliyense, ndipo kodi m’bale wako anaikidwa kuno kuti iweyo udzigobere manda kunoko?’+ Iye wagoba manda ake pamwamba pa phiri lamiyala. Akudzikonzera malo opumulirako m’thanthwe.

  • Ezekieli 26:20
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 20 ndidzakutsitsira m’dzenje, ngati mmene ndinatsitsira ena onse m’manda momwe muli anthu amene anafa kalekale.+ Ine ndidzakuchititsa kukhala pansi, panthaka.+ Udzakhala kumeneko pamodzi ndi malo ena amene anawonongedwa kalekale ndiponso pamodzi ndi ena onse amene akutsikira kumanda.+ Ndidzachita zimenezi kuti anthu asadzakhalenso mwa iwe, koma m’dziko la anthu amoyo ndidzaikamo zokongoletsera.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena