Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Salimo 22:22
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 22 Ndidzalengeza dzina lanu+ kwa abale anga.+

      Ndidzakutamandani pakati pa mpingo.+

  • Salimo 40:9
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  9 Ndanena za uthenga wabwino wachilungamo mumpingo waukulu.+

      Onani! Sindinatseke pakamwa panga.+

      Inu Yehova, mukudziwa bwino zimenezi.+

  • Salimo 111:1
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 111 Tamandani Ya, anthu inu!+

      א [ʼAʹleph]

      Ndidzatamanda Yehova ndi mtima wanga wonse,+

      ב [Behth]

      Pakati pa gulu+ la owongoka mtima ndi pamsonkhano wawo.+

  • Aheberi 2:12
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 12 pamene akunena kuti: “Ndidzalengeza dzina lanu kwa abale anga. Ndidzakutamandani mwa kuimba nyimbo pakati pa mpingo.”+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena