Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • 2 Samueli 16:12
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 12 Mwina Yehova aona+ ndi diso lake, ndipo lero Yehova abwezeretsa kwa ine zinthu zabwino m’malo mwa temberero la Simeyi.”+

  • Salimo 39:7
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  7 Nanga tsopano, inu Yehova, ine ndikuyembekezera chiyani?

      Chiyembekezo changa chili mwa inu.+

  • Salimo 123:2
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  2 Taonani! Monga mmene maso a atumiki amayang’anira dzanja la mbuye wawo,+

      Mmene maso a kapolo wamkazi amayang’anira dzanja la mbuye wake wamkazi,+

      Momwemonso, maso athu adzayang’ana kwa Yehova Mulungu wathu,+

      Kufikira atatikomera mtima.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena