Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Numeri 23:19
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 19 Mulungu si munthu, woti anganene mabodza,+

      Si mwana wa munthu, woti angadzimve kuti ali ndi mlandu.+

      Kodi ananenapo kanthu koma osachita,

      Analankhulapo kanthu kodi koma osakwaniritsa?+

  • Salimo 73:11
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 11 Iwo anena kuti: “Mulungu angadziwe bwanji?+

      Kodi Wam’mwambamwamba akudziwa zimenezi?”+

  • Salimo 94:7
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  7 Iwo amanena kuti: “Ya sakuona,+

      Ndipo Mulungu wa Yakobo sakudziwa zimene zikuchitika.”+

  • Mlaliki 8:12
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 12 Ngakhale woipa atachita zoipa+ maulendo 100 n’kukhala ndi moyo wautali akuchitabe zofuna zake, ine ndikudziwa kuti anthu amene amaopa Mulungu woona zidzawayendera bwino,+ chifukwa chakuti anali kumuopa.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena