Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Genesis 6:12
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 12 Chotero, Mulungu poyang’ana dziko lapansi anaona kuti laipa,+ chifukwa njira za anthu onse zinali zitaipa.+

  • Salimo 12:1
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 12 Ndipulumutseni,+ inu Yehova, pakuti anthu okhulupirika atha.+

      Anthu okhulupirika atheratu pakati pa ana a anthu.

  • Salimo 14:3
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  3 Onse apatuka,+ ndipo onsewo ndi achinyengo.+

      Palibe aliyense amene akuchita zabwino,+

      Palibiretu ndi mmodzi yemwe.+

  • Mlaliki 7:20
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 20 Palibe munthu wolungama padziko lapansi amene amachita zabwino zokhazokha osachimwa.+

  • Aroma 3:12
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 12 Anthu onse apanduka, onse pamodzi akhala opanda pake. Palibe amene akusonyeza kukoma mtima, palibiretu ndi mmodzi yemwe.”+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena