Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Yobu 9:4
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  4 Iye ali ndi mtima wanzeru ndiponso mphamvu zambiri.+

      Ndani angachite naye makani,* koma osavulala?+

  • Salimo 63:2
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  2 Choncho ndakuonani m’malo oyera,+

      Chifukwa ndaona mphamvu zanu ndi ulemerero wanu.+

  • Salimo 77:14
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 14 Inu ndinu Mulungu woona amene mukuchita zodabwitsa.+

      Mphamvu zanu mwazidziwikitsa pakati pa mitundu ya anthu.+

  • Nahumu 1:3
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 3 Yehova sakwiya msanga+ ndipo ali ndi mphamvu zambiri,+ komatu Yehova salephera kulanga wolakwa.+

      Njira yake ili mumphepo yowononga ndi mumphepo yamkuntho. Mitambo ndilo fumbi lopondapo mapazi ake.+

  • Chivumbulutso 19:1
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 19 Zimenezi zitatha, ndinamva mawu ofuula kumwamba+ ngati mawu a khamu lalikulu, akuti: “Tamandani Ya,* anthu inu!+ Chipulumutso,+ ulemerero, ndi mphamvu ndi za Mulungu wathu,+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena