Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Salimo 11:2
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  2 Pakuti oipa akunga uta,+

      Akonzekeretsa mivi yawo kuti aiponye ndi uta,

      Kuti alase anthu owongoka mtima kuchokera pamalo amdima.+

  • Salimo 58:7
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  7 Asungunuke ndi kupita ngati madzi.+

      Mulungu akunge uta woponyera mivi yake pamene adaniwo akugwa.+

  • Yeremiya 9:8
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 8 Lilime lawo ndiwo muvi wophera anthu.+ Limalankhula chinyengo chokhachokha. Munthu aliyense amalankhula mwamtendere ndi mnzake, koma mumtima mwake amakonza chiwembu.”+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena