Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Salimo 42:8
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  8 Masana Yehova adzalamula kukoma mtima kwake kosatha kuti kufike pa ine,+

      Ndipo usiku ndidzaimba za iye.+

      Ndidzapemphera kwa Mulungu wondipatsa moyo.+

  • Salimo 71:3
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  3 Mukhale thanthwe lachitetezo loti ndizilowamo nthawi zonse.+

      Lamulani kuti ndipulumutsidwe,+

      Pakuti inu ndinu thanthwe langa ndi malo anga achitetezo.+

  • Yesaya 40:31
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 31 koma anthu odalira+ Yehova adzapezanso mphamvu.+ Iwo adzaulukira m’mwamba ngati ali ndi mapiko a chiwombankhanga.+ Adzathamanga koma osafooka. Adzayenda koma osatopa.”+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena