Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Salimo 22:6
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  6 Koma ine ndine nyongolotsi+ osati munthu.

      Anthu amanditonza ndipo ndine wonyozeka kwa anthu.+

  • Salimo 44:22
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 22 Koma chifukwa cha inu, tikuphedwa nthawi zonse.

      Takhala ngati nkhosa zokaphedwa.+

  • Yeremiya 15:15
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 15 Inu Yehova mukudziwa bwino mavuto anga.+ Ndikumbukireni+ ndipo mutembenuke ndi kundiyang’ana kuti mubwezere anthu ondizunza.+ Musandichotsere moyo wanga chifukwa chakuti simupsa mtima mwamsanga.+ Onani chitonzo chimene chili pa ine chifukwa cha dzina lanu.+

  • Mateyu 5:11
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 11 “Ndinu odala pamene anthu akukunyozani+ ndi kukuzunzani,+ komanso kukunamizirani zoipa zilizonse chifukwa cha ine.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena