Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Deuteronomo 11:19
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 19 Ana anu muwaphunzitsenso mawu amenewa, ndipo muzilankhula nawo za mawuwa mukakhala pansi m’nyumba mwanu, poyenda pamsewu, pogona ndi podzuka.+

  • Salimo 71:8
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  8 M’kamwa mwanga mwadzaza mawu otamanda inu,+

      Ndipo pakamwa panga pakunena za ulemerero wanu tsiku lonse.+

  • Miyambo 10:20
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 20 Lilime la wolungama ndilo siliva wabwino kwambiri.+ Mtima wa woipa ndi wopanda phindu.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena