Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Deuteronomo 33:27
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 27 Mulungu wakale lomwe ndiwo malo ako obisalamo,+

      Ndipo iwe uli m’manja amene adzakhalapo mpaka kalekale.+

      Adzapitikitsa mdani pamaso pako,+

      Ndipo adzanena kuti, ‘Awononge!’+

  • Salimo 91:1
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 91 Aliyense wokhala m’malo otetezeka+ a Wam’mwambamwamba+

      Adzakhala wosungika mumthunzi wa Wamphamvuyonse.+

  • Chivumbulutso 21:3
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 3 Kenako ndinamva mawu ofuula kuchokera kumpando wachifumu, akuti: “Taonani! Chihema+ cha Mulungu chili pakati pa anthu. Iye adzakhala pamodzi nawo,+ ndipo iwo adzakhala anthu ake.+ Zoonadi, Mulunguyo adzakhala nawo.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena