Yobu 30:30 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 30 Khungu langa linakhala lakuda+ ndipo linayoyoka pathupi panga.Mafupa anga anatentha chifukwa chouma. Salimo 31:10 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 10 Chifukwa cha chisoni, moyo wanga watha,+Ndipo chifukwa cha kuusa moyo kwanga, zaka zanga zafika kumapeto.+Chifukwa cha zolakwa zanga, mphamvu zanga zafooka,+Ndipo mafupa anga afooka.+ Maliro 1:13 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 13 Iye watumiza moto m’mafupa+ mwanga kuchokera kumwamba, ndipo wafooketsa fupa lililonse.Watchera ukonde+ kuti ukole mapazi anga. Wandibweza kumbuyo.Wandisandutsa mkazi wosiyidwa popanda thandizo. Ndikudwala tsiku lonse.+
30 Khungu langa linakhala lakuda+ ndipo linayoyoka pathupi panga.Mafupa anga anatentha chifukwa chouma.
10 Chifukwa cha chisoni, moyo wanga watha,+Ndipo chifukwa cha kuusa moyo kwanga, zaka zanga zafika kumapeto.+Chifukwa cha zolakwa zanga, mphamvu zanga zafooka,+Ndipo mafupa anga afooka.+
13 Iye watumiza moto m’mafupa+ mwanga kuchokera kumwamba, ndipo wafooketsa fupa lililonse.Watchera ukonde+ kuti ukole mapazi anga. Wandibweza kumbuyo.Wandisandutsa mkazi wosiyidwa popanda thandizo. Ndikudwala tsiku lonse.+