Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Yobu 19:6
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  6 Dziwani kuti Mulungu mwiniwakeyo ndi amene wandisocheretsa,

      Ndipo wandizunguliza ndi ukonde wake wosakira nyama.+

  • Salimo 66:11
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 11 Mwatilowetsa mu ukonde wosakira nyama,+

      Mwatinyamulitsa katundu wolemera m’chiuno mwathu.

  • Ezekieli 12:13
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 13 Ine ndidzamutambasulira ukonde wanga. Chotero iye adzakodwa mu ukonde wanga wosakira+ ndipo ndidzamupititsa ku Babulo, kudziko la Akasidi.+ Koma iye sadzaliona ndipo adzafera komweko.+

  • Ezekieli 17:20
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 20 Ndidzam’ponyera ukonde wanga ndipo adzakodwa mu ukonde wanga wosakira.+ Ndiyeno ndidzamubweretsa ku Babulo ndi kumuweruza chifukwa chondichitira zinthu mosakhulupirika.+

  • Hoseya 7:12
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 12 “Kulikonse kumene iwo angapite, ndidzawatchera ndi ukonde.+ Ndidzawagwira ngati zolengedwa zouluka m’mlengalenga.+ Ndidzawalanga mogwirizana ndi chenjezo limene ndinauza msonkhano wawo.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena