Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Deuteronomo 32:15
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 15 Yesuruni*+ atayamba kunenepa, anayamba kupanduka.+

      Iwe wanenepa, wakulupala, wakhuta mopitirira muyezo.+

      Pamenepo iye anasiya Mulungu amene anam’panga,+

      Ndi kunyoza Thanthwe+ la chipulumutso chake.

  • Salimo 119:70
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  70 Mitima yawo yauma ngati mafuta oundana,+

      Koma ine ndimakonda chilamulo chanu.+

  • Ezekieli 16:49
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 49 ‘Tamvera! Cholakwa cha m’bale wako Sodomu chinali, kunyada,+ kukhala ndi chakudya chokwanira+ ndiponso kukhala ndi moyo wabata+ ndi wosatekeseka. Izi n’zimene iye ndi midzi yake yozungulira anali nazo.+ Sanalimbitse dzanja la munthu wosautsika+ ndi wosauka.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena