Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Yobu 13:4
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  4 Koma amuna inu ndinu onamizira anzanu.+

      Nonsenu ndinu madokotala opanda phindu.+

  • Salimo 86:14
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 14 Inu Mulungu, anthu odzitukumula andiukira.+

      Khamu la anthu opondereza anzawo likufunafuna moyo wanga,+

      Ndipo sanakuikeni patsogolo pawo.+

  • Salimo 109:2
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  2 Munthu woipa ndiponso munthu wachinyengo andinenera zoipa ndi pakamwa pawo.+

      Iwo anena za ine ndi lilime lonama.+

  • Salimo 119:51
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  51 Anthu odzikuza andinyoza koopsa.+

      Koma ine sindinapatuke pa chilamulo chanu.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena