1 Samueli 24:2 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 2 Pamenepo Sauli anatenga amuna osankhidwa mwapadera 3,000+ mu Isiraeli monse, ndipo anapita kukafunafuna Davide+ ndi amuna amene anali kuyenda naye m’matanthwe amene mumakhala mbuzi za m’mapiri.+ Salimo 10:8 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 8 Iye amabisalira anthu pafupi ndi midzi.Amabisalira munthu wosalakwa ndi kumupha.+ ע [ʽAʹyin]Maso ake amafunafuna waumphawi.+ Salimo 37:32 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 32 Woipa amalondalonda munthu wolungama,+Ndipo amafuna kuti amuphe.+ Mateyu 26:4 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 4 Iwo anali kupangana+ zoti agwire Yesu mochenjera ndi kumupha. Machitidwe 23:21 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 21 Koma chonde musalole kuti akunyengerereni, pakuti amuna oposa 40 akumudikirira panjira.+ Amenewa achita kulumbira modzitemberera kuti sadya kapena kumwa kanthu kufikira atamupha.+ Moti panopa akonzeka, akungoyembekezera chilolezo chanu.”
2 Pamenepo Sauli anatenga amuna osankhidwa mwapadera 3,000+ mu Isiraeli monse, ndipo anapita kukafunafuna Davide+ ndi amuna amene anali kuyenda naye m’matanthwe amene mumakhala mbuzi za m’mapiri.+
8 Iye amabisalira anthu pafupi ndi midzi.Amabisalira munthu wosalakwa ndi kumupha.+ ע [ʽAʹyin]Maso ake amafunafuna waumphawi.+
21 Koma chonde musalole kuti akunyengerereni, pakuti amuna oposa 40 akumudikirira panjira.+ Amenewa achita kulumbira modzitemberera kuti sadya kapena kumwa kanthu kufikira atamupha.+ Moti panopa akonzeka, akungoyembekezera chilolezo chanu.”