Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Salimo 25:15
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 15 Maso anga amayang’ana kwa Yehova nthawi zonse,+

      Chifukwa iye ndi amene amawonjola phazi langa mu ukonde.+

  • Salimo 121:1
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 121 Ndakweza maso anga kuyang’ana kumapiri.+

      Kodi thandizo langa lichokera kuti?+

  • Salimo 141:8
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  8 Koma ine maso anga ali pa inu+ Yehova Ambuye Wamkulu Koposa.+

      Ndathawira kwa inu.+

      Musalole kuti moyo wanga uwonongeke.+

  • Luka 18:13
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 13 Koma wokhometsa msonkho uja, ataima chapatali ndithu, sanafune ngakhale kukweza maso ake kumwamba. Anali kungodziguguda pachifuwa+ ndi kunena kuti, ‘Mulungu wanga, ndikomereni mtima munthu wochimwa ine.’+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena