Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • 2 Mbiri 20:12
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 12 Inu Mulungu wathu kodi simuwaweruza?+ Ifeyo patokha tilibe mphamvu zotha kulimbana ndi khamu lalikulu limene likubwera kudzamenyana nafeli+ ndipo sitikudziwa chochita,+ koma maso athu ali pa inu.”+

  • Salimo 25:15
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 15 Maso anga amayang’ana kwa Yehova nthawi zonse,+

      Chifukwa iye ndi amene amawonjola phazi langa mu ukonde.+

  • Salimo 123:1
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 123 Ndakweza maso anga kuyang’ana inu,+

      Kuyang’ana inu amene mukukhala kumwamba.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena