Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • 2 Mafumu 19:26
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 26 Anthu okhala m’mizindayo adzafooka manja.+

      Adzachita mantha kwambiri ndiponso adzachita manyazi.+

      Adzakhala ngati zomera zakutchire, ndi udzu wanthete wobiriwira,+

      Ngati udzu womera padenga+ ukawauka ndi mphepo yotentha yakum’mawa.+

  • Nehemiya 4:4
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 4 Ndiyeno Nehemiya anati: “Inu Mulungu wathu, imvani+ mawu onyoza amene akutinenera.+ Bwezerani chitonzo chawocho+ pamutu pawo ndipo apititseni m’dziko laukapolo monga zofunkha.

  • Salimo 37:2
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  2 Pakuti adzafota mwamsanga ngati udzu,+

      Adzanyala ngati msipu watsopano wobiriwira.+

  • Salimo 92:7
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  7 Anthu oipa akamaphuka ngati msipu,+

      Ndipo anthu onse ochita zopweteka anzawo akamaphuka ngati maluwa,

      Amatero kuti awonongeke kwamuyaya.+

  • Yesaya 37:27
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 27 Anthu okhala m’mizindayo adzafooka manja.+

      Adzachita mantha kwambiri ndiponso adzachita manyazi.+

      Adzakhala ngati zomera zakutchire, ndi udzu wanthete wobiriwira,+

      Ngati udzu womera padenga+ ndiponso wa m’mizere ya m’munda, ukawauka ndi mphepo yotentha yakum’mawa.+

  • Yeremiya 17:6
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 6 Adzakhala ngati mtengo umene uli pawokhawokha m’chipululu ndipo zabwino zikadzafika sadzatha kuziona.+ Iye adzakhala m’malo ouma a m’chipululu m’dziko la nthaka yamchere, kumene sikukhala anthu.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena