Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • 2 Samueli 7:3
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 3 Pamenepo Natani anauza mfumu kuti: “Chitani chilichonse chimene chili mumtima mwanu,+ chifukwa Yehova ali nanu.”

  • Salimo 22:25
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 25 Chifukwa cha zimene mwachita ndidzakutamandani mumpingo waukulu.+

      Ndidzakwaniritsa malonjezo anga pamaso pa anthu oopa iye.+

  • Salimo 46:11
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 11 Yehova wa makamu ali ndi ife.+

      Mulungu wa Yakobo ndiye malo athu okwezeka ndiponso achitetezo.+ [Seʹlah.]

  • Salimo 61:8
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  8 Choncho ndidzaimba nyimbo zotamanda dzina lanu mpaka muyaya,+

      Kuti ndikwaniritse malonjezo anga tsiku ndi tsiku.+

  • Salimo 146:5
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  5 Wodala ndi munthu amene thandizo lake limachokera kwa Mulungu wa Yakobo,+

      Amene chiyembekezo chake chili mwa Yehova Mulungu wake,+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena