Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Yobu 38:25
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 25 Ndani anagawa ngalande ya madzi osefukira,

      Ndi njira ya mtambo wa mvula yamabingu,+

  • Salimo 147:8
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  8 Muimbireni Iye amene amaphimba mapiri ndi mitambo,+

      Amene amakonza mvula kuti igwe padziko lapansi,+

      Amenenso amameretsa udzu wobiriwira m’mapiri.+

  • Zekariya 10:1
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 10 “Pemphani Yehova kuti akugwetsereni mvula+ pa nthawi ya mvula yomalizira.+ Pemphani Yehova amene anapanga mitambo yamvula+ ndiponso amene amagwetsera anthu mvula yamphamvu.+ Iye amapereka mbewu m’munda mwa munthu aliyense.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena