Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Yobu 38:27
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 27 Kuti inyowetse malo owonongeka ndi mvula yamkuntho ndiponso ouma,

      Komanso kuti imeretse udzu?+

  • Salimo 104:14
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 14 Amameretsa msipu kuti nyama zidye,+

      Ndipo amameretsa mbewu kuti anthu agwiritse ntchito.+

      Amachita zimenezi kuti chakudya chituluke m’nthaka,+

  • Yesaya 30:23
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 23 Mulungu adzabweretsa mvula pambewu zanu zimene munabzala munthaka,+ ndipo zokolola za munthakayo zidzakhala chakudya chopatsa thanzi.+ M’tsiku limenelo, ziweto zanu zidzadya msipu pamalo aakulu odyetserapo ziweto.+

  • Zekariya 10:1
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 10 “Pemphani Yehova kuti akugwetsereni mvula+ pa nthawi ya mvula yomalizira.+ Pemphani Yehova amene anapanga mitambo yamvula+ ndiponso amene amagwetsera anthu mvula yamphamvu.+ Iye amapereka mbewu m’munda mwa munthu aliyense.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena