Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Deuteronomo 32:36
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 36 Pakuti Yehova adzaweruza anthu ake,+

      Ndipo adzamva chisoni chifukwa cha atumiki ake,+

      Chifukwa adzaona kuti thandizo lawachokera.

      Adzaona kuti pangokhala munthu wonyozeka ndi wopanda pake.

  • 1 Mbiri 21:15
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 15 Kuwonjezera pamenepo, Mulungu woona anatumiza mngelo ku Yerusalemu kuti akawononge mzindawo.+ Mngeloyo atangoyamba kuwononga, Yehova anaona zimenezo ndi kumva chisoni chifukwa cha tsokalo,+ choncho anauza mngelo amene anali kuwonongayo kuti: “Basi pakwanira!+ Tsitsa dzanja lako tsopano.” Pa nthawiyi, mngelo wa Yehova uja anali ataimirira pafupi ndi malo opunthira mbewu a Orinani+ Myebusi.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena