Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Yoswa 1:8
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 8 Buku la malamulo ili lisachoke pakamwa pako,+ uziliwerenga ndi kusinkhasinkha usana ndi usiku, kuti uonetsetse kuti ukutsatira zonse zolembedwamo.+ Pakuti ukatero, udzakhala ndi moyo wopambana, ndipo udzachita zinthu mwanzeru.+

  • Salimo 35:28
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 28 Lilime langa linene chapansipansi za chilungamo chanu,+

      Ndipo likutamandeni tsiku lonse.+

  • Salimo 119:97
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  97 Ndimakonda kwambiri chilamulo chanu!+

      Ndimasinkhasinkha chilamulocho tsiku lonse.+

  • 1 Timoteyo 4:15
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 15 Sinkhasinkha zinthu zimenezi mozama.+ Dzipereke pa zinthu zimenezi kuti anthu onse aone kuti ukupita patsogolo.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena