Salimo 119:72 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 72 Chilamulo+ chotuluka pakamwa panu n’chabwino kwa ine,+N’chabwino kwambiri kuposa ndalama masauzande zagolide ndi zasiliva.+ Mateyu 5:17 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 17 “Musaganize kuti ndinabwera kudzawononga Chilamulo+ kapena Zolemba za aneneri. Sindinabwere kudzaziwononga koma kudzazikwaniritsa.+ Luka 2:22 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 22 Komanso, masiku akuti iwo ayeretsedwe+ malinga ndi chilamulo cha Mose atakwanira, anapita naye ku Yerusalemu kukam’pereka kwa Yehova. Aroma 2:13 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 13 Pajatu akumva chabe chilamulo si amene amakhala olungama pamaso pa Mulungu, koma otsatira+ chilamulo ndiwo adzayesedwa olungama.+ Aroma 7:14 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 14 Pakuti tikudziwa kuti Chilamulo n’chauzimu,+ koma ine ndine wakuthupi, wogulitsidwa ku uchimo.+ Aroma 7:22 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 22 Mumtima mwanga+ ndimasangalala kwambiri+ ndi chilamulo cha Mulungu, Aroma 9:31 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 31 Koma ngakhale kuti Aisiraeli anali kutsatira lamulo la chilungamo, sanalipeze lamulolo.+
72 Chilamulo+ chotuluka pakamwa panu n’chabwino kwa ine,+N’chabwino kwambiri kuposa ndalama masauzande zagolide ndi zasiliva.+
17 “Musaganize kuti ndinabwera kudzawononga Chilamulo+ kapena Zolemba za aneneri. Sindinabwere kudzaziwononga koma kudzazikwaniritsa.+
22 Komanso, masiku akuti iwo ayeretsedwe+ malinga ndi chilamulo cha Mose atakwanira, anapita naye ku Yerusalemu kukam’pereka kwa Yehova.
13 Pajatu akumva chabe chilamulo si amene amakhala olungama pamaso pa Mulungu, koma otsatira+ chilamulo ndiwo adzayesedwa olungama.+