Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Yobu 9:10
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 10 Amachita zinthu zazikulu ndi zosatheka kuzifufuza,+

      Ndiponso zinthu zodabwitsa zosawerengeka.+

  • Yobu 26:14
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 14 Komatu zimenezi ndi kambali kakang’ono chabe ka zochita zake,+

      Ndipo timangomva kunong’ona kwapansipansi kwa mawu ake.

      Koma kodi mabingu ake amphamvu, angawamvetse ndani?”+

  • Yobu 36:26
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 26 Mulungu ndi wokwezeka kuposa mmene tikudziwira.+

      Zaka zake n’zosawerengeka.+

  • Salimo 92:5
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  5 Ntchito zanu ndi zazikuludi inu Yehova!+

      Maganizo anu ndi ozama kwambiri.+

  • Salimo 139:6
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  6 Kwa ine ndi zovuta kwambiri kuti ndidziwe zinthu zonsezi.+

      Ndi zapamwamba kwambiri moti sindingathe kuzifikira.+

  • Aroma 11:33
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 33 Ndithudi, madalitso amene Mulungu amapereka ndi ochuluka kwambiri.+ Nzeru+ zake n’zozama, ndiponso iye ndi wodziwa zinthu kwambiri.+ Ziweruzo zake ndi zosasanthulika,+ ndipo ndani angatulukire njira zake?

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena