Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Salimo 65:4
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  4 Wodala ndi munthu amene inu mwamusankha ndi kumuyandikizitsa kwa inu,+

      Kuti akhale m’mabwalo anu.+

      Tidzakhutira ndi zinthu zabwino za m’nyumba yanu,+

      Malo anu oyera kapena kuti kachisi wanu woyera.+

  • Salimo 92:5
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  5 Ntchito zanu ndi zazikuludi inu Yehova!+

      Maganizo anu ndi ozama kwambiri.+

  • Mlaliki 3:11
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 11 Chilichonse iye anachipanga chokongola ndiponso pa nthawi yake.+ Komanso anapatsa anthu mtima wofuna kukhala ndi moyo mpaka kalekale+ kuti ntchito imene Mulungu woona wagwira, iwo asaidziwe kuyambira pa chiyambi mpaka pa mapeto.+

  • Yesaya 55:9
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 9 “Pakuti monga momwe kumwamba kulili pamwamba kuposa dziko lapansi,+ momwemonso njira zanga n’zapamwamba kuposa njira zanu,+ ndiponso maganizo anga ndi apamwamba kuposa maganizo anu.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena