Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Yobu 42:3
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  3 Inu munati, ‘Kodi amene akuphimba malangizo anga mopanda nzeruyu ndani?’+

      Chotero ine ndinalankhula, koma sindinali kuzindikira

      Zinthu zodabwitsa kwambiri kwa ine, zimene sindikuzidziwa.+

  • Salimo 40:5
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  5 Inu Yehova Mulungu wanga, mwatichitira zinthu zambiri zodabwitsa,+

      Ndipo mumatiganizira.+

      Palibe angafanane ndi inu.+

      Ndikafuna kulankhula ndi kunena za zodabwitsazo,

      Zimachuluka kwambiri moti sindingathe kuzifotokoza.+

  • Salimo 131:1
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 131 Inu Yehova, mtima wanga sunadzikweze,+

      Maso anga si onyada.+

      Sindinafune zinthu zapamwamba kwambiri,+

      Kapena zinthu zodabwitsa kwambiri.+

  • Aroma 11:33
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 33 Ndithudi, madalitso amene Mulungu amapereka ndi ochuluka kwambiri.+ Nzeru+ zake n’zozama, ndiponso iye ndi wodziwa zinthu kwambiri.+ Ziweruzo zake ndi zosasanthulika,+ ndipo ndani angatulukire njira zake?

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena