Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Salimo 25:8
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  8 Yehova ndi wabwino ndi wolungama.+

      N’chifukwa chake amalangiza ochimwa kuti ayende m’njira yoyenera.+

  • Salimo 100:5
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  5 Pakuti Yehova ndi wabwino.+

      Kukoma mtima kwake kosatha kudzakhalapo mpaka kalekale,+

      Ndipo kukhulupirika kwake kudzakhalapo ku mibadwomibadwo.+

  • Salimo 104:28
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 28 Zimalandira zimene mwazipatsa.+

      Mumatambasula dzanja lanu ndipo zimakhutira ndi zinthu zabwino.+

  • Nahumu 1:7
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 7 Yehova ndi wabwino+ ndipo ndi malo achitetezo+ pa tsiku la nsautso.+

      Amadziwa amene amathawira kwa iye kuti apeze chitetezo.+

  • Mateyu 5:45
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 45 kuti musonyeze kuti ndinudi ana a Atate wanu wakumwamba.+ Chifukwa iye amawalitsira dzuwa lake pa anthu oipa ndi abwino, ndi kuvumbitsira mvula anthu olungama ndi osalungama omwe.+

  • Machitidwe 14:17
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 17 Komabe iye sanangokhala wopanda umboni wakuti anachita zabwino.+ Anakupatsani mvula+ kuchokera kumwamba ndi nyengo zimene zokolola zanu zimakhala zambiri. Anadzaza mitima yanu ndi chakudya komanso chimwemwe.”+

  • Yakobo 1:17
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 17 Mphatso iliyonse yabwino+ ndi yangwiro imachokera kumwamba,+ pakuti imatsika kuchokera kwa Atate wa zounikira zonse zakuthambo,+ ndipo iye sasintha ngati kusuntha kwa mthunzi.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena