Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • 2 Mbiri 20:8
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 8 Ndiyeno iwo anayamba kukhalamo ndipo anakumangirani malo opatulika a dzina lanu m’dzikolo,+ n’kunena kuti,

  • Salimo 29:9
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  9 Liwu la Yehova likuchititsa mbawala zazikazi kuphiriphitha ndi ululu wa pobereka,+

      Ndipo likufafaniza nkhalango.+

      M’kachisi wake aliyense akunena kuti: “Ulemerero ndi wa Mulungu!”+

  • Salimo 116:19
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 19 M’mabwalo a nyumba ya Yehova,+

      Pakati pa iwe Yerusalemu.+

      Tamandani Ya, anthu inu!+

  • Salimo 134:2
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  2 Pamene mukupemphera mutakweza manja anu, muzikhala oyera,+

      Ndipo tamandani Yehova.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena