Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Salimo 59:6
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  6 Madzulo amabweranso.+

      Ndipo amauwa ngati agalu+ ndi kuzungulira mzinda wonse.+

  • Luka 22:63
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 63 Tsopano amuna amene anagwira Yesu aja anayamba kumuchitira zachipongwe,+ ndi kumumenya.+

  • Afilipi 3:2
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 2 Chenjerani ndi agalu.+ Chenjerani ndi ochita ntchito zovulaza. Chenjerani ndi anthu amene amachita mdulidwe.+

  • Chivumbulutso 22:15
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 15 Kunja kuli anthu amene ali ngati agalu,+ amene amachita zamizimu,+ adama,+ opha anthu, opembedza mafano, ndi aliyense wokonda kulankhula ndi kuchita zachinyengo.’+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena