Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Yobu 34:29
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 29 Iye akachititsa bata, ndani angamudzudzule?

      Ndipo akabisa nkhope yake,+ ndani angamuone?

      Kaya abisire nkhope yake mtundu+ kapena munthu, n’chimodzimodzi.

  • Salimo 10:1
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 10 N’chifukwa chiyani inu Yehova mukuima kutali?+

      N’chifukwa chiyani mukubisala pa nthawi ya masautso?+

  • Salimo 143:7
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  7 Fulumirani, ndiyankheni inu Yehova.+

      Mphamvu zanga zatha.+

      Musandibisire nkhope yanu,+

      Chifukwa mukatero ndikhala ngati anthu amene akutsikira kudzenje la manda.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena