Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Genesis 49:18
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 18 Ndithu ndidzayembekezera chipulumutso kwa inu, Yehova.+

  • Salimo 62:1
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 62 Ndithudi, moyo wanga ukuyembekezera Mulungu modekha.+

      Chipulumutso changa chidzachokera kwa iye.+

  • Salimo 71:14
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 14 Koma ine ndidzayembekezera inu nthawi zonse,+

      Ndipo ndidzakutamandani mowirikiza kuposa kale.

  • Maliro 3:21
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 21 Ndidzakumbukira zimenezi mumtima mwanga.+ Pa chifukwa chimenechi, ndidzakhala ndi mtima wodikira.+

  • Mika 7:7
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 7 Koma ine ndidzadikirira Yehova.+ Ndidzayembekezera moleza mtima Mulungu wa chipulumutso changa.+ Mulungu wanga adzandimvera.+

  • Tito 2:13
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 13 Tizichita zimenezi pamene tikuyembekeza kukwaniritsidwa kwa chiyembekezo+ chosangalatsa ndi kuonetsedwa kwaulemerero+ kwa Mulungu wamkuluyo ndiponso kwa Mpulumutsi wathu, Khristu Yesu.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena