Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Yobu 30:10
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 10 Akunyansidwa nane, ndipo akukhala patali ndi ine.+

      Sakuzengereza kundilavulira kumaso.+

  • Miyambo 14:20
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 20 Munthu wosauka amadedwa ngakhale ndi mnzake,+ koma munthu wolemera amakhala ndi anzake ambiri.+

  • Yakobo 2:6
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 6 Koma inu simulemekeza munthu wosauka. Kodi si olemera amene amakusautsani+ ndi kukukokerani kumabwalo amilandu?+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena