Deuteronomo 16:20 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 20 Uzitsatira chilungamo.+ Ndithudi uzitsatira chilungamo kuti ukhale ndi moyo ndi kukatengadi dziko limene Yehova Mulungu wako akukupatsa.+ Yobu 21:28 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 28 Popeza mukuti, ‘Kodi nyumba ya wolemekezeka ili kuti,Ndipo hema wa oipa ali kuti? Kodi malo awo okhala ali kuti?’+ Salimo 37:10 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 10 Patsala kanthawi kochepa, woipa sadzakhalakonso.+Udzayang’ana pamene anali kukhala, ndipo sadzapezekapo.+ Salimo 91:8 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 8 Udzayang’ana ndi maso ako,+Ndipo udzaona anthu oipa akulandira chilango.+ Salimo 101:8 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 8 M’mawa uliwonse ndidzawononga oipa onse a padziko lapansi.+Ndidzapha ndi kuchotsa mumzinda wa Yehova anthu onse ochita zinthu zopweteka anzawo.+
20 Uzitsatira chilungamo.+ Ndithudi uzitsatira chilungamo kuti ukhale ndi moyo ndi kukatengadi dziko limene Yehova Mulungu wako akukupatsa.+
28 Popeza mukuti, ‘Kodi nyumba ya wolemekezeka ili kuti,Ndipo hema wa oipa ali kuti? Kodi malo awo okhala ali kuti?’+
10 Patsala kanthawi kochepa, woipa sadzakhalakonso.+Udzayang’ana pamene anali kukhala, ndipo sadzapezekapo.+
8 M’mawa uliwonse ndidzawononga oipa onse a padziko lapansi.+Ndidzapha ndi kuchotsa mumzinda wa Yehova anthu onse ochita zinthu zopweteka anzawo.+