Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Miyambo 10:1
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 10 Miyambi ya Solomo.+

      Mwana wanzeru amakondweretsa bambo ake,+ koma mwana wopusa amamvetsa chisoni mayi ake.+

  • Miyambo 15:20
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 20 Mwana wanzeru ndi amene amakondweretsa bambo ake,+ koma wopusa amanyoza mayi ake.+

  • Miyambo 27:11
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 11 Mwana wanga, khala wanzeru ndi kukondweretsa mtima wanga,+ kuti ndimuyankhe amene akunditonza.+

  • Luka 1:14
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 14 Udzakondwa ndi kusangalala kwambiri, ndipo ambiri adzasangalala+ ndi kubadwa kwake

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena