Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Salimo 34:15
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 15 Maso a Yehova ali pa olungama,+

      Ndipo makutu ake amamva kufuula kwawo kopempha thandizo.+

  • Salimo 145:19
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 19 Ndipo anthu amene amamuopa adzawachitira zokhumba zawo,+

      Adzamva kufuula kwawo kopempha thandizo ndipo adzawapulumutsa.+

  • Yesaya 58:9
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 9 Chotero inu mudzaitana ndipo Yehova adzakuyankhani. Mudzafuula popempha+ ndipo iye adzayankha kuti, ‘Ndikumva lankhulani!’

      “Mukachotsa goli pakati panu,+ mukaleka kutosana chala+ ndi kulankhulana zopweteka,+

  • Yohane 9:31
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 31 Tikudziwa kuti Mulungu samvetsera ochimwa,+ koma ngati munthu ali woopa Mulungu ndipo amachita chifuniro chake, ameneyo amamumvetsera.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena