Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Genesis 27:41
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 41 Choncho, Esau anasunga chidani kwa Yakobo mumtima mwake.+ Anamuda chifukwa cha madalitso amene bambo ake anamupatsa. Iye anapitiriza kunena mumtima mwake+ kuti: “Masiku olira maliro a bambo anga ali pafupi.+ Pambuyo pake, ndidzamupha m’bale wanga Yakobo.”+

  • 2 Samueli 13:22
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 22 Abisalomu sanalankhule chilichonse, chabwino kapena choipa kwa m’bale wake Aminoni, pakuti Abisalomu anadana+ ndi Aminoni chifukwa chochititsa manyazi Tamara mlongo wake.

  • 1 Mafumu 2:23
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 23 Mfumu Solomo itatero, inalumbira pamaso pa Yehova kuti: “Mulungu andilange mowirikiza+ ngati Adoniya sanaike moyo wake pangozi mwa kupempha zimenezi.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena