Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Salimo 69:20
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 20 Mtima wanga wasweka chifukwa cha chitonzo, ndipo chilonda chake ndi chosachiritsika.+

      Ndinali kuyembekezera kuti wina andimvere chifundo, koma panalibe ndi mmodzi yemwe,+

      Ndinali kuyembekezera onditonthoza, koma sanapezeke ngakhale mmodzi.+

  • Salimo 142:4
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  4 Yang’anani kudzanja lamanja ndipo muone

      Kuti palibe aliyense amene akufuna kundithandiza.+

      Ndilibenso malo othawirako,+

      Ndipo palibe amene akufunsa za moyo wanga.+

  • 2 Timoteyo 4:16
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 16 Pamene ndinali kudziteteza koyamba pa mlandu wanga, palibe amene anakhala kumbali yanga. Onse anandisiya ndekha.+ Ngakhale zinali choncho, usakhale mlandu kwa iwo.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena