Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Salimo 31:11
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 11 Ndakhala chitonzo+ pamaso pa onse odana nane,+

      Ndipo kwa anthu oyandikana nawo ndakhala chitonzo chachikulu,+

      Kwa anthu ondidziwa ndakhala woopsa.+

      Akandiona ndili panja amandithawa.+

  • Salimo 69:20
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 20 Mtima wanga wasweka chifukwa cha chitonzo, ndipo chilonda chake ndi chosachiritsika.+

      Ndinali kuyembekezera kuti wina andimvere chifundo, koma panalibe ndi mmodzi yemwe,+

      Ndinali kuyembekezera onditonthoza, koma sanapezeke ngakhale mmodzi.+

  • Salimo 88:8
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  8 Anzanga mwawaika kutali ndi ine.+

      Mwandisandutsa chinthu chonyansa kwa iwo.+

      Ndatsekerezedwa ndipo sindingathenso kuchoka.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena