Yobu 19:13 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 13 Iye waika abale anga enieni kutali ndi ine,+Ndipo ngakhale anthu ondidziwa andisiya. Yobu 19:19 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 19 Amuna onse amene anali anzanga apamtima akudana nane,+Ndipo amene ndinali kuwakonda anditembenukira.+ Salimo 31:11 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 11 Ndakhala chitonzo+ pamaso pa onse odana nane,+Ndipo kwa anthu oyandikana nawo ndakhala chitonzo chachikulu,+Kwa anthu ondidziwa ndakhala woopsa.+Akandiona ndili panja amandithawa.+ Salimo 142:4 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 4 Yang’anani kudzanja lamanja ndipo muoneKuti palibe aliyense amene akufuna kundithandiza.+Ndilibenso malo othawirako,+Ndipo palibe amene akufunsa za moyo wanga.+ Luka 23:49 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 49 Komanso onse amene anali kumudziwa anaimirira chapatali ndithu.+ Ndipo amayi amene anamutsatira kuchokera ku Galileya, anaimiriranso chapomwepo n’kumaonerera zinthu zimenezi.+
19 Amuna onse amene anali anzanga apamtima akudana nane,+Ndipo amene ndinali kuwakonda anditembenukira.+
11 Ndakhala chitonzo+ pamaso pa onse odana nane,+Ndipo kwa anthu oyandikana nawo ndakhala chitonzo chachikulu,+Kwa anthu ondidziwa ndakhala woopsa.+Akandiona ndili panja amandithawa.+
4 Yang’anani kudzanja lamanja ndipo muoneKuti palibe aliyense amene akufuna kundithandiza.+Ndilibenso malo othawirako,+Ndipo palibe amene akufunsa za moyo wanga.+
49 Komanso onse amene anali kumudziwa anaimirira chapatali ndithu.+ Ndipo amayi amene anamutsatira kuchokera ku Galileya, anaimiriranso chapomwepo n’kumaonerera zinthu zimenezi.+