Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Nehemiya 7:2
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 2 Zitatero ndinaika Haneni+ m’bale wanga ndi Hananiya kalonga wa m’Nyumba ya Chitetezo Champhamvu,+ kuti aziyang’anira Yerusalemu. Hananiya anali munthu wodalirika+ ndipo anali woopa kwambiri+ Mulungu woona kuposa anthu ena ambiri.

  • Yobu 33:23
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 23 Ngati iye ali ndi mthenga,

      Womulankhulira mmodzi pa omulankhulira 1,000,

      Kuti auze munthu zimene zili zowongoka,

  • Salimo 12:1
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 12 Ndipulumutseni,+ inu Yehova, pakuti anthu okhulupirika atha.+

      Anthu okhulupirika atheratu pakati pa ana a anthu.

  • Afilipi 2:20
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 20 Pakuti ndilibe wina wamtima ngati iye, amene angasamaledi+ za inu moona mtima.

  • 2 Petulo 2:8
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 8 Munthu wolungama ameneyo anali kuzunzika tsiku ndi tsiku ndi zimene anali kuona ndi kumva pamene anali kukhala pakati pawo, ndiponso chifukwa cha zochita zawo zosamvera malamulo.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena