Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Genesis 31:40
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 40 Ndinkangokhalira kutenthedwa ndi dzuwa usana ndi kuzizidwa ndi mphepo usiku, ndipo tulo sindinkationa.+

  • Danieli 6:18
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 18 Kenako mfumu inapita kunyumba yake yachifumu. Usiku umenewo mfumuyo inasala kudya+ ndipo sanaiimbire nyimbo ndi zipangizo zoimbira, komanso sinathe kugona tulo.+

  • Luka 12:29
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 29 Choncho lekani kudera nkhawa za chimene mudzadya ndi chimene mudzamwa, ndipo siyani kuvutika mumtima.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena