Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Salimo 7:17
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 17 Ndidzatamanda Yehova chifukwa cha chilungamo chake.+

      Ndidzaimba nyimbo motsatizana ndi zipangizo zoimbira, kutamanda dzina+ la Yehova Wam’mwambamwamba.+

  • Salimo 99:5
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  5 Kwezani Yehova Mulungu wathu+ ndipo muweramireni pachopondapo mapazi ake.+

      Iye ndi woyera.+

  • Salimo 145:1
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 145 Ndidzakukwezani, inu Mfumu ndi Mulungu wanga,+

      Ndipo ndidzatamanda dzina lanu mpaka kalekale, ndithu mpaka muyaya.+

  • Aheberi 13:15
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 15 Kudzera mwa iye, tiyeni nthawi zonse tizitamanda Mulungu. Tizichita zimenezi monga nsembe imene tikupereka kwa Mulungu,+ yomwe ndi chipatso cha milomo yathu.+ Timagwiritsa ntchito milomo imeneyi polengeza dzina lake kwa anthu ena.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena