Salimo 35:28 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 28 Lilime langa linene chapansipansi za chilungamo chanu,+Ndipo likutamandeni tsiku lonse.+ Salimo 51:14 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 14 Inu Mulungu, ndilanditseni ku mlandu wa magazi,+ inu Mulungu wa chipulumutso changa,+Kuti lilime langa linene za chilungamo chanu mokondwera.+ Salimo 71:15 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 15 Pakamwa panga padzanena za chilungamo chanu,+Padzanena za chipulumutso chanu tsiku lonse,+Pakuti ntchito za chilungamo ndi chipulumutso chanu ndi zochuluka ndipo sindinathe kuziwerenga.+ Salimo 98:2 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 2 Yehova wachititsa chipulumutso chake kudziwika.+Chilungamo chake wachisonyeza ku mitundu ya anthu.+ Salimo 145:7 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 7 Iwo adzalankhula mosefukira za kuchuluka kwa ubwino wanu,+Ndipo adzafuula mokondwera chifukwa cha chilungamo chanu.+
14 Inu Mulungu, ndilanditseni ku mlandu wa magazi,+ inu Mulungu wa chipulumutso changa,+Kuti lilime langa linene za chilungamo chanu mokondwera.+
15 Pakamwa panga padzanena za chilungamo chanu,+Padzanena za chipulumutso chanu tsiku lonse,+Pakuti ntchito za chilungamo ndi chipulumutso chanu ndi zochuluka ndipo sindinathe kuziwerenga.+
2 Yehova wachititsa chipulumutso chake kudziwika.+Chilungamo chake wachisonyeza ku mitundu ya anthu.+
7 Iwo adzalankhula mosefukira za kuchuluka kwa ubwino wanu,+Ndipo adzafuula mokondwera chifukwa cha chilungamo chanu.+