Yesaya 7:25 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 25 Kumapiri onse amene anthu anali kulambulako ndi makasu kuti achotse zomera zovutitsa, sadzapitakonso chifukwa choopa tchire la zitsamba zaminga ndi udzu. Malowo adzakhala odyetserako ng’ombe zamphongo ndi opondapondako nkhosa.”+ Yesaya 17:2 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 2 Mizinda ya Aroweri+ imene yasiyidwa m’mbuyo yangosanduka malo okhala ziweto, kumene ziwetozo zimagona pansi popanda woziopsa.+ Yesaya 32:14 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 14 Pakuti nsanja yokhalamo yasiyidwa,+ piringupiringu amene anali mumzindamo watha. Ofeli+ ndi nsanja ya mlonda zasanduka tchire. Mpaka kalekale zidzakhala malo osangalalako mbidzi, ndi odyetserako ziweto,
25 Kumapiri onse amene anthu anali kulambulako ndi makasu kuti achotse zomera zovutitsa, sadzapitakonso chifukwa choopa tchire la zitsamba zaminga ndi udzu. Malowo adzakhala odyetserako ng’ombe zamphongo ndi opondapondako nkhosa.”+
2 Mizinda ya Aroweri+ imene yasiyidwa m’mbuyo yangosanduka malo okhala ziweto, kumene ziwetozo zimagona pansi popanda woziopsa.+
14 Pakuti nsanja yokhalamo yasiyidwa,+ piringupiringu amene anali mumzindamo watha. Ofeli+ ndi nsanja ya mlonda zasanduka tchire. Mpaka kalekale zidzakhala malo osangalalako mbidzi, ndi odyetserako ziweto,