Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Numeri 32:34
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 34 Tsopano ana a Gadi anayamba kumanga mizinda ya Diboni,+ Ataroti,+ Aroweli,+

  • Yoswa 13:16
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 16 Dziko lawo linayambira ku Aroweli,+ mzinda umene uli m’mphepete mwa chigwa cha Arinoni, ndiponso mzinda umene uli pakati pa chigwacho. Dzikoli linaphatikizapo malo onse okwererapo apafupi ndi Medeba,+

  • 2 Mafumu 10:33
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 33 Anayambira ku Yorodano chakotulukira dzuwa, dziko lonse la Giliyadi,+ Agadi,+ Arubeni+ ndi Amanase,+ kuyambira ku Aroweli+ yemwe ali pafupi ndi chigwa* cha Arinoni, ngakhalenso Giliyadi ndi Basana.+

  • Yeremiya 48:19
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 19 “Ima chilili ndi kuona zimene zikuchitika m’njira, iwe mkazi wokhala ku Aroweli.+ Funsa mwamuna ndi mkazi amene akuthawa. Uwafunse kuti, ‘Chachitika n’chiyani?’+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena