Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Yesaya 29:15
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 15 Tsoka kwa anthu amene abisa patali kwambiri zolinga zawo, pozibisira Yehova,+ amene zochita zawo zimachitikira m’malo a mdima,+ ndipo amati: “Ndani akutiona, ndipo ndani akudziwa zimene tikuchita?”+

  • Hoseya 4:10
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 10 Iwo adzadya koma sadzakhuta.+ Adzachita zachiwerewere ndi akazi koma sadzachulukana+ chifukwa chakuti asiya kumvera Yehova.+

  • 1 Atesalonika 4:8
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 8 Choncho munthu wonyalanyaza+ chiphunzitso chimenechi sakunyalanyaza munthu, koma Mulungu+ amene amaika mzimu wake woyera+ mwa inu.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena