Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Salimo 8:9
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  9 Inu Yehova Ambuye wathu, dzina lanu ndi lalikulu padziko lonse lapansi!+

  • Salimo 93:4
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  4 Ulemerero wa Yehova ndi waukulu+ kumwamba,

      Kuposa mkokomo wa madzi ambiri, kuposanso mafunde amphamvu a m’nyanja.+

  • Luka 9:43
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 43 Pamenepo, onse anadabwa ndi mphamvu zodabwitsa+ za Mulungu.

      Tsopano onse adakali odabwa ndi zonse zimene anali kuchita, Yesu anauza ophunzira ake kuti:

  • Aheberi 8:1
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 8 Ndiye kunena za zinthu zimene tikukambiranazi, mfundo yaikulu ndi iyi: Tili ndi mkulu wa ansembe+ ngati ameneyu, ndipo iye wakhala pansi kumwamba, kudzanja lamanja la mpando wachifumu wa Wolemekezeka.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena