Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Salimo 74:10
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 10 Inu Mulungu, kodi mdani adzakuchitirani mopanda ulemu kufikira liti?+

      Kodi mdani adzanyoza dzina lanu kwamuyaya?+

  • Salimo 79:12
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 12 Bwezerani anthu oyandikana nafe mwa kuwatsanulira chitonzo pachifuwa pawo maulendo 7,+

      Inu Yehova, muwabwezere chitonzo chimene anachita pa inu.+

  • Yesaya 37:4
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 4 Mwina Yehova Mulungu amva mawu onse a Rabisake,+ amene mbuye wake mfumu ya Asuri yamutuma, kuti adzatonze+ nawo Mulungu wamoyo. Ndipo mwina amulanga chifukwa cha mawu amene Yehova Mulungu wanu wamva.+ Inuyo mupereke pemphero+ m’malo mwa otsalira amene alipo.’”+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena